Ambuye George Desmond Tambala, Arkiepiskopi wa Arkidayosizi yaKatolika ya Lilongwe, apempha zipani za ansembe komanso ma sisitele mu arkidayosiziyi kuti afikire achinyamata m’maparishi osiyanasiyana ndi cholinga choti azimvetsesa nkhani za mayitanidwe. Ambuye Tambala ayankhula izi la Mulungu la Mayitanidwe, 21 April 2024 ku Parishi ya Mlare pa mwambo wa nsembe ya misa yomwe achinyamata mu… Continue reading AMBUYE TAMBALA APEMPHA ZIPANI ZAMUMPINGO KUFIKIRA ACHINYAMATA KU MAPARISHI AWO
AMBUYE TAMBALA APEMPHA ZIPANI ZAMUMPINGO KUFIKIRA ACHINYAMATA KU MAPARISHI AWO
