Don Bosco Youth Technical Institute has on 22 April 2024 hosted the launch of communication strategy in the country as one of the countries under Don Bosco Tech-Africa. Malawi has become the first country to launch the communication strategy out of the 11 countries which are under the Don Bosco Tech Africa. Speaking at the […]
Ambuye George Desmond Tambala, Arkiepiskopi wa Arkidayosizi yaKatolika ya Lilongwe, apempha zipani za ansembe komanso ma sisitele mu arkidayosiziyi kuti afikire achinyamata m’maparishi osiyanasiyana ndi cholinga choti azimvetsesa nkhani za mayitanidwe. Ambuye Tambala ayankhula izi la Mulungu la Mayitanidwe, 21 April 2024 ku Parishi ya Mlare pa mwambo wa nsembe ya misa yomwe achinyamata mu […]
Bungwe la Centre for Agricultural Transformation (CAT) lapempha alimi m’dziko muno kuyamba kubzala mbeu ya maungu akuluakulu (Giant Pumpkins) ndi cholinga chofuna kuchepetsa njala yomwe imakuta dziko lino chaka ndi chaka. Izi zayankhulidwa lachisanu pa 16 February 2024 pamwambo wachionetsero cha mbewu ya mawunguyi, yomwe ikutchedwa NRC Giant Pumpkin, yomwe inalimidwa miyezi ingapo yapitayi ku […]
Wolemba ndi Sam Kalimba Arkidayosizi ya Lilongwe yayamikira ndi kulimbikitsa a sistere a chipani cha Missionaries of Mary Mediatrix (M.M.M) kamba ka utumiki wawo womwe ati akuwugwira modziyiwala mu Arkidayosiziyi. Arkiepisikopi wa Arkidayosiziyi George Desmond Tambala ndiwo ayankhula izi pa mbuyo pa mwambo wa Misa ya malumbiro oyamba a Sr. Apronia Mahowe ndi Sr. Stella […]
By Tiyamike Chisale The new Catholic Bishop in Malawi, Rt. Rev. Vincent Mwakhwawa has highlighted the need for the youth to respond to their vocations in accordance with what their hearts suggest. Bishop Mwakhwawa made the sentiments on Sunday 28th January 2023 at St. Paul Parish in Nkhotakota during his thanksgiving Mass at his home […]
Government has asked traditional leaders in the country to lead in uniting the citizenry in order for the country to prosper. Minister of Local Government and Unity, honorable Richard Chimwemdo Banda made the remarks on Thursday 28th December 2023 during the elevation of Traditional Authority (TA) M’bwatalika to Senior TA M’bwatalika at Mtunthumala headquarters. Chimwendo […]